

Goals
Fear God, and give glory to Him
Proclaiming the Everlasting Gospel in the Spirit of the Three Angels
End Time Messengers is a fellowship proclaiming the everlasting gospel and preparing believers for Christ’s return through the message of Revelation 14:7–12. Join us as we study, pray, and live by Heaven’s truth in these final days.
Habakkuk 2:1
Ndidzaima pa dindiro langa ndi kudziika palinga, ndipo ndidzayang'anira ndione ngati adzanenanji mwa ine, ngatinso ndidzamyankha ciani pa coneneza canga.
Tilipati Mu Ulosi
Tikufuna mulingilire mwakuya.... Kuti mukabwerako bwanji? Mmene anthu akulimvera kukoma dzikoli?
A global call to truth and worship

Romans 10:17
"So the faith cometh by hearing, and hearing by the word of God."
Faith is not born from mere belief or emotion—it grows through hearing the Word of God. Every message, every teaching, and every moment spent in His Word strengthens our trust in Him. As we listen, our hearts open to His truth, and our lives are transformed by His promises.
Let us, therefore, make it our daily pursuit to hear, understand, and live by God’s Word, for through it, faith takes root and flourishes.
Chibvumbulutso-147-10; Opani Mulungu, mpatseni ulemerero; pakuti yafika nthawi ya ciweruziro cace; ndipo mlambireni iye amene analenga m'mwamba ndi mtunda ndi nyanja ndi akasupe amadzi, `Ndipo anatsata mngelo wina mnzace ndi kunena, Wagwa, wagwa, Babulo waukuru umene unamwetsako mitundu yonse ku vinyo wa mkwiyo wa cigololo cace.