Revelation 14:7

Fear God and give glory to Him; for the hour of His judgment is come.

Worship God sincerely from the heart, live righteously by following His truth, honor Him as Creator of all things, and always remember that every action is accountable before His holy and divine authority..

Read More

Follow Us :

services4
mathew_24-removebg-preview-300x300

Goals

Matthew 24:14
And this gospel of the kingdom shall be preached in all the world for a witness unto all nations; and then shall the end come.
The global spread of truth is the final sign before Christ’s return.

Fear God, and give glory to Him

Proclaiming the Everlasting Gospel in the Spirit of the Three Angels

End Time Messengers is a fellowship proclaiming the everlasting gospel and preparing believers for Christ’s return through the message of Revelation 14:7–12. Join us as we study, pray, and live by Heaven’s truth in these final days.

Habakkuk 2:1

Ndidzaima pa dindiro langa ndi kudziika palinga, ndipo ndidzayang'anira ndione ngati adzanenanji mwa ine, ngatinso ndidzamyankha ciani pa coneneza canga.

Tilipati Mu Ulosi

Tikufuna mulingilire mwakuya.... Kuti mukabwerako bwanji? Mmene anthu akulimvera kukoma dzikoli?

Kodi mumadziwa kuti chisautso chikuchedwa chifukwa inu ndi ine sitikulalikira?
Tangolingalirani: tsiku lina mudzuke mudziyenda nkhomo ndi khomo osasakha kaya ili ku mpanda ndi mau awa:
ZOKHUDZA GULULI
Pakuti ici ncokoma ndi colandirika pamaso pa Mulungu Mpulumutsi wathu; amene afuna anthu onse apulumuke, nafike pozindikira coonadi. 1 Timoteyo 2:4
KODI MUMADZIWA?
Ambiri timaoneka ngati Okhulupilira pamene TIKUKHALA pakati pa Okhulupilira * KUSAKHULUPILIRA sikuyezedwa chifukwa cha kusakana kupitana nawo ku ntchito ko, koma kukagwira ntchito yomwe mwapitirayo ndiye nkhani
MASOMPHENYA AWA NDIWO CHILIMBIKITSO CHA UTUMIKI UWU
Habakkuk 2:1 Ndidzaima pa dindiro langa ndi kudziika palinga, ndipo ndidzayang'anira ndione ngati adzanenanji mwa ine, ngatinso ndidzamyankha ciani pa coneneza canga.

A global call to truth and worship

Prophecies

Understanding God’s Plan for the End of Time

SERMONS

Messages of Hope, Faith, and Readiness for Christ’s Return

HEALTH

Honoring God Through a Wholesome and Balanced Life

FARMING

Working the Soil as Stewards of God’s Creation

Events

Moments of Fellowship, Learning, and Revival

NEWSLETTERS

Staying Informed, Strengthened, and United in Faith

RADIO

Kukweza chiyembekezo cha moyo wanu wosatha

News

Current world events aren’t random, they are fulfilling prophecy and preparing the world for Christ’s return.

Hope Amid Uncertainty

The end-time message is not of despair, but of hope, redemption, and victory (John 16:33)

Roman-10
Romans 10:17
"So the faith cometh by hearing, and hearing by the word of God."
Faith is not born from mere belief or emotion—it grows through hearing the Word of God. Every message, every teaching, and every moment spent in His Word strengthens our trust in Him. As we listen, our hearts open to His truth, and our lives are transformed by His promises. Let us, therefore, make it our daily pursuit to hear, understand, and live by God’s Word, for through it, faith takes root and flourishes.

Chibvumbulutso-147-10; Opani Mulungu, mpatseni ulemerero; pakuti yafika nthawi ya ciweruziro cace; ndipo mlambireni iye amene analenga m'mwamba ndi mtunda ndi nyanja ndi akasupe amadzi, `Ndipo anatsata mngelo wina mnzace ndi kunena, Wagwa, wagwa, Babulo waukuru umene unamwetsako mitundu yonse ku vinyo wa mkwiyo wa cigololo cace.